Mai wina adabwisa anthu ndi khalidwe lake
Mai wapa mudzi wina kwa Chikowi m’boma la Zomba akudabwitsa anthu kamba ka khalidwe lake.
Mwamuna wina adabwitsa anthu pa maliro
Mwamuna wina pa mudzi wina kwa Kachere m’boma la Dedza wadabwitsa anthu pa maliro a mwana wake.
Anyanyalilidwa mwana ku ntchito
Mwamuna wina yemwe amagwira ntchito ku bungwe lina kwa Chimwaye kwa Kwataine m’boma la Ntcheu anazingwa mkazi wake atamunyanyalira mwana wa miyezi itatu ku ntchito.
Bambo wina amuminitsa ku Lilongwe
Bambo wina yemwe wakhala akunyozera kupita ku maliro a nzake amuminitsa ku Area 49 mu mzinda wa Lilongwe.