Omvera paja pali mau oti magwiragwira amapha manja. Nkhaniyi yapherezera mdera la Mzukuzuku ku Mzimba pamene mnyamata wina wayamba kulankhula zosamveka atakaba mtondo wapa banja lina.
Mwamuna wina kwa Ganya m’boma la Ntcheu zamusokonekera mkazi wa chibwezi atamulanda foni.
Mwamuna wina ku Migowi m’boma la Phalombe yemwe anali pa ubwenzi wa ntseri ndi mkazi wamwini wachimina.
Ntchembere zina ku Fatima m’dera la mfumu Mlolo m’boma la Nsanje zinakalipira mai wina wa mwana m’modzi poyankhula zoduka mutu pagulu.