Agogo awili okalamba kwambili akunthana kwambili kwa Mchinguza mboma la Machinga mpaka kutsala pang’ono kusokoneza mwambo wachinamwali cha jando.
Achinyamata ena anai ku Maleule kwa Kapeni m’boma la Blantyre anawamangilira pa mtengo ku manda kamba kosokoneza pa maliro.
Achinyamata ena anai ku Maleule kwa Kapeni m’boma la Blantyre anawamangilira pa mtengo ku manda kamba kosokoneza pa maliro.
Mwamuna wina kwa Gulupu Kalungwe mdera la Likoswe m’boma la Chiradzulu wanenetsa kuti wachimina atamugwiritsa ntchito yonse yapa mwambo osesa.