Anthu ena atatu akuwaloza chala powaganizira kuti akuphunzitsa ana zinthu zachilendo kwa Nankumba ku Monkay Bay, m’boma la Mangochi.
Mwamuna wina mdera la Chigalu ku Blantyre anaona ngati kutulo atagwidwa ali chino-chino kuseli kwa uvuni.
Mwamuna wina mdera la Kachere ku Dedza wasamuka mderalo chifukwa cha utambwali.
Mwamuna wina mdera la Kachere ku Dedza wasamuka mderalo chifukwa cha utambwali.