Panja lina lisekedwa
Banja lina akuliseka pa sitolo za kwa Nkanda m’boma la Mchinji. Nkhaniyi ikuti masiku apita mkulu wina yemwe ndi wochita malonda pamalopo anapezerela mkazi wake akutchaya lamya kwa mwamumuna wachibwenzi.
Mkazi wa abusa asowa mtendere
Mkazi wa m’busa wina akusowa mtendere mdera la Chimaliro m’boma la Thyolo. Yemwe watumiza nkhaniyi wati mderalo muli msing’anga wina wazitsamba yemwe ali ndi akazi oposa atatu.
Chidakwa china chikupidwa makofi
Chidakwa china pa Neno Turn off m’boma la Neno chaona polekera atachithambitsa ndi makofi owonetsa nyenyezi.
Apasidwa makofi kamba kofuna kudzimangilira
Mwamuna wina mdera la Mitundu ku Lilongwe waona polekera atamuthambitsa ndi makofi chifukwa chofuna kudzimangilira.