Adyetsa mamuna khuzumule kamba kowilikiza zadama
Mai wina kwa Chinsapo mu mzinda wa Lilongwe wadyetsa mwamuna wake khuzumule atatopa ndi nkhalidwe la mchiuno la mwamuna-yo.
Banja likunthana kamba ka alendo
Mu mzinda wa Blantyre omwe-wo ku Malingamoyo banja lina linamenyana modetsa nkhawa mwamuna wa mnyumba-mo atakwiya kuti akuchikazi afika pa khomo-po kukacheza.
Maliro ayenda pa ngolo
Maliro a mkulu wina kwa Kayembe mboma la Dowa anayenda pa ngolo potsatila malamulo omwe mkulu-yo ananena ali moyo.
Atemedwa kuchibwenzi
M’nyamata wina wa geni ku Chigwirizano ku Lilongwe amutema ku chibwenzi, atakumana ndi mwini mkazi yemwe amazembelana naye.