You are here:CategoriesNkhani Zam'maboma
22
July

22/07/15

Written by
Published in Nkhani Zam'maboma
Read 2419 times

Adyetsa mamuna khuzumule kamba kowilikiza zadama
Mai wina kwa Chinsapo mu mzinda wa Lilongwe wadyetsa mwamuna wake khuzumule atatopa ndi nkhalidwe la mchiuno la mwamuna-yo.

22
July

21/07/15

Written by
Published in Nkhani Zam'maboma
Read 2237 times

Banja likunthana kamba ka alendo
Mu mzinda wa Blantyre omwe-wo ku Malingamoyo banja lina linamenyana modetsa nkhawa mwamuna wa mnyumba-mo atakwiya kuti akuchikazi afika pa khomo-po kukacheza.

22
July

20/07/15

Written by
Published in Nkhani Zam'maboma
Read 2224 times

Maliro ayenda pa ngolo
Maliro a mkulu wina kwa Kayembe mboma la Dowa anayenda pa ngolo potsatila malamulo omwe mkulu-yo ananena ali moyo.

21
July

19/07/15

Written by
Published in Nkhani Zam'maboma
Read 2117 times

Atemedwa kuchibwenzi
M’nyamata wina wa geni ku Chigwirizano ku Lilongwe amutema ku chibwenzi, atakumana ndi mwini mkazi yemwe amazembelana naye.

About us

Malawi Broadcasting Corporation is a public broadcaster mandated and formed by Government under an Act of Parliament in 1964, to enhance the successful implementation of all its social and economic programs...

Social Media

Catch us on these social networks for more information

Facebook Twitter RSS

Get Your Newsletter