Aletsedwa kulemba mayeso a std8
Anthu a m’mudzi wa Ng’ombezalira kwa Kaphuka mboma la Dedza ati ndiwokhumudwa komanso odabwa ndi zomwe achita akuluakulu owona za maphunzilo mderalo poletsa mtsikana wina wa std 8 kulemba nawo mayeso a chaka chino.
Akolola chimanga cha eni
Mwamuna wina wapa mudzi wa Ndalama kwa Chitera m’boma la Chiradzulu yemwe wakwatira pa mudzi wa Malinga m’bomalo akuyenda wera-wera ngati wataya singano atamugwira akukolola chimanga m’munda mwa mbale wake.
Kazizi tsakamuka kudenga pamapemphero
Mapemphero anasokonezeka mu mpingo wina kwa mfumu Kalonga m’boma la Salima , Kadzidzi wakufa atatsakamuka kudenga nkugwera m’busa yemwe amalalikira.
Amenya mayi ake kamba komanidwa nsima
Mnyamata wina wa Kumtumanje m’boma la Zomba wathawa atamenya mai ake mpaka kukomoka chifukwa choti mai akewo anamumana msima.